Saturday, January 17, 2015

REST IN PEACE BISHOP JOSEPH MUKASA ZUZA

Death Announcement
BISHOP JOSEPH MUKASA ZUZA
The Catholic Secretariat of the Episcopal Conference of Malawi regrets to
announce the tragic death of Rite Reverend Bishop Joseph Mukasa Zuza, who was
bishop of Mzuzu Diocese and Chairman for the Episcopal Conference of Malawi
(ECM).
According to report, Bishop Zuza was involved in a road accident and has
passed on while being attended in Mzuzu.
More information and details shall follow later.
MAY HIS SOUL REST IN ETERNAL PEACE
____________________________________________
UTHENGA WACHISONI
AMBUYE JOSEPH MUKASA ZUZA
Bungwe la Maepiskopi a Mpingo Wa Katolika - Episcopal Conference of Malawi
(ECM) – ili ndi chisoni kukudziwitsani za imfa ya Olemekezeka Ambuye Joseph
Mukasa ZUZA amene anali episkopi wa Dayosizi ya Mzuzu komanso Wapampando
wa Bungwe la Maepiskopi aKatolika m’Malawi (ECM).
Malinga ndi uthenga umene talandira, Ambuye Zuza anachita ngozi ya
galimoto ndipo amwalira pamene anali kulandira hithandizo kuchipatala ku Mzuzu.
Fr Andrew KAUFA
COMMUNICATIONS SECRETARY – ECM
Death Announcement
BISHOP JOSEPH MUKASA ZUZA
The Catholic Secretariat of the Episcopal Conference of Malawi regrets to
announce the tragic death of Rite Reverend Bishop Joseph Mukasa Zuza, who was
bishop of Mzuzu Diocese and Chairman for the Episcopal Conference of Malawi
(ECM).
According to report, Bishop Zuza was involved in a road accident and has
passed on while being attended in Mzuzu.
More information and details shall follow later.
MAY HIS SOUL REST IN ETERNAL PEACE
____________________________________________
UTHENGA WACHISONI
AMBUYE JOSEPH MUKASA ZUZA
Bungwe la Maepiskopi a Mpingo Wa Katolika - Episcopal Conference of Malawi
(ECM) – ili ndi chisoni kukudziwitsani za imfa ya Olemekezeka Ambuye Joseph
Mukasa ZUZA amene anali episkopi wa Dayosizi ya Mzuzu komanso Wapampando
wa Bungwe la Maepiskopi aKatolika m’Malawi (ECM).
Malinga ndi uthenga umene talandira, Ambuye Zuza anachita ngozi ya
galimoto ndipo amwalira pamene anali kulandira hithandizo kuchipatala ku Mzuzu.
Fr Andrew KAUFA
COMMUNICATIONS SECRETARY – ECM

No comments: